DRIEMO Compensation cover image

Compensation Lyrics

Compensation Lyrics by DRIEMO


Kuti mwina compensation
Driemo
Ndidzapereke moyo wanga

Oh mtima uwupereke, kwaine ndiwutenge
Don't you worry about safety
Ndidzachengetera chengetera chengetera
I know mtima unaswekapo
You've been there unalirapo, ululu mumtima kufikapo
Ukaganizira ganizira ganizira
Paiwe ndilola ndipepere, chikondi chisaperewere
Olo pa ground paterere I will love you the same baby

Oh udzandifunse
Ndikadzakuswera mtima udzandifunse
Kuti mwina compensation
Ndidzapereke moyo wanga
Oh udzandifunse
Ndikadzakuswera mtima udzandifunse
Kuti mwina compensation
Ndidzapereke moyo wanga

Don't be scared to love me more
Zakale zapita it's me and you
Undiuze pomwe Pali mantha ako
I know mtima umakana ukandiunika
Umaona ngati Aja anakunamiza koma
I wanna be your soldier
Your fighter
Protector
Defender
I just wanna be your friend for life

Oh udzandifunse
Ndikadzakuswera mtima udzandifunse
Kuti mwina compensation
Ndidzapereke moyo wanga
Oh udzandifunse
Ndikadzakuswera mtima udzandifunse
Kuti mwina compensation
Ndidzapereke moyo wanga

Ooh udzandifunse
Udzandifunse, mwina compensation ndidzapereke moyo wanga eeee

Oh udzandifunse
Ndikadzakuswera mtima udzandifunse
Kuti mwina compensation
Ndidzapereke moyo wanga
Oh udzandifunse
Ndikadzakuswera mtima udzandifunse
Kuti mwina compensation
Ndidzapereke moyo wanga

Watch Video

About Compensation

Album : Compensation (Single)
Release Year : 2022
Added By : Farida
Published : Aug 27 , 2022

More DRIEMO Lyrics

DRIEMO
DRIEMO
DRIEMO

Comments ( 0 )

No Comment yet



About AfrikaLyrics

Afrika Lyrics is the most diverse collection of African song lyrics and translations. Afrika Lyrics provides music lyrics from over 30 African countries and lyrics translations from over 10 African Languages into English and French

Follow Afrika Lyrics

© 2024, We Tell Africa Group Sarl