...

Kadigong Lyrics by SHO MADJOZI


Moni moni moni

Kuyilowa ndi mutu

Ndasiya mudothi

Mayazi maya mayazi

Gwira malaya nane ndi ilowe basi

Mayazi mayazi mayazi

Kuyilowa ndi mutu mopanda manyazi

Maya mayazi mayazi

Nkhani yamanyado ilbe n’khala pakati

Mayazi mayazi mayazi

Okudya ndalama samatcheka balansi

Vina

Tchola

Tshika

Kadi gong

Sinali plani kuti ndikukonde (Koma)

watshekemela ngati ndiwe combe (Ona)

Watseleekeza ma guy wonse

odi ndi ka pote

Tizitchiiilla tiKhale Pa easy

Ndili ndi mandede ngati Iani lizzi

Ndimakoonda njonda zachimidzi

A/khale wauleemu opanda utchissi

Tenga u/moodzi tinyowe kukhosi

(Nane ndima/nyowa uka/kamba zaku\khosi )

Ndikutengele ku/Jhoni u/kawone tshotshi (jozi)**q

U/kazipeza /ndi achina Sho madJozi konkoo

Ndi/libe phuma ndine nkazi wodeekha

Koma ndi Kabwella undi/vulile wekha

Mfana woteentha ta/ziiyiteleka

ku/mayi chakulila ndika/mayi peleka

Vina

Tchola

Tshika

Kadi gong

Mkazi wakunja khalidwe lachimalawi

Ndipanga naye chani fukwa ndine mphawi

Nyumba yakwawo yaku mayadi

Makolo akachoka timapanga party

Chikondi cha season ngati mtengo wa mango

Koma ndatopa nane ndikhale wako

Uzi ndigwira gwira ngati kupanga chipako

Polama pango’no undigwiritse thako

Ndikukwatile kapena tipange chinkhoswe

Olo ndidzidya mwa chinsinsi ngati khoswe

Dona ya ulemu Ndipo alibe chipongwe

Ndimupatse mimba kuti akhale pakhonde

Wabwera ndi Bola odi ndikapote

Tikawone Nyanja Ng’ona ku liwonde

Kukunyaditsa kuti akuwone

A Nsanje ka

Watch Video

About Kadigong

Album : (Single)
Release Year : 2024
Copyright :
Added By : Farida
Published : Oct 15 , 2024

More SHO MADJOZI Lyrics

SHO MADJOZI
SHO MADJOZI
SHO MADJOZI
SHO MADJOZI

Comments ( 0 )

No Comment yet



About AfrikaLyrics

Afrika Lyrics is the most diverse collection of African song lyrics and translations. Afrika Lyrics provides music lyrics from over 30 African countries and lyrics translations from over 10 African Languages into English and French

Follow Afrika Lyrics

© 2024, We Tell Africa Group Sarl