Njala Lyrics by GODDY ZAMBIA


Ne nibakonda alume angu
Nao onikonda, ovutikila banja yasu
Kuti tisakafwe nanjala ah! Ah! Ah!
Mwepeza nchito kukalale
Pe mwenzoluta mwenzeti mukawele
Lomba papita masiku anyinji
Bana balila njala ne nibape chinji?

Njala njala njala ahh njala mukawele liti?
Njala njala ahh njala njala njala mukawele liti?

Kuno mai ndinabwelera zanchito koma zonse ziti kuno kulibetu nchito
Ndina dikhira kufikira zakudya ndinatengazo zinata panjila
Ndalama zinagwa twenty kwacha ndinasala nayo yo inata
Ndinkhatumiza koma ten kwacha ndiyo ndinkasala nayo
Ndizayetsetsa kukongola kwa anzangu
Basi ndikatero nditumiza osadanda ndimagobo ndikumenya kuno ndi anzanga
Zikakwana zokwerera ine ndizachika
Kufika kuchika kufika kuchika kwathu konko
Kufika kuchika konko
Ndizafika kuchika kufika kuchika kwathu konko kufika kuchika konko

Njala njala njala ahh njala mukawele liti?
Njala njala ahh njala njala njala mukawele liti?

Ana ali bwanji? Inu muli bwanji?
Agogo mukukhala nawo kodi muli bwanji ? Ehhh
Mukaone amake dalitso,kuli chomwe ndatumiza konko kuli mavuto
mukufa njala ana njala ati mbuto zakubzyala munadya chiwaya
Ehh ija nkongole anatengako sabina inu tandiuza sanalete sarafina?
Njala njala njala njala ndidziwa mukufa njala
Koma ndikubwera konko posachedwa.

Njala njala njala ahh njala mukawele liti?
Njala njala ahh njala njala njala mukawele liti?
Eh njala ahh njala mukawele liti?
Njala aah njala aah mukawele liti?

Ndizafika kuchika kufika kuchika kwathu konko
Kufika kuchika konko
(njala njala njala ah ah ah mukawele liti?)

Watch Video

About Njala

Album : Njala (Single)
Release Year : 2022
Added By : Farida
Published : Mar 02 , 2022

More GODDY ZAMBIA Lyrics

Comments ( 0 )

No Comment yet



About AfrikaLyrics

Afrika Lyrics is the most diverse collection of African song lyrics and translations. Afrika Lyrics provides music lyrics from over 30 African countries and lyrics translations from over 10 African Languages into English and French

Follow Afrika Lyrics

© 2024, We Tell Africa Group Sarl